Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 2:52 - Buku Lopatulika

52 Ndipo Yesu anakulabe m'nzeru ndi mumsinkhu, ndi m'chisomo cha pa Mulungu ndi cha pa anthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

52 Ndipo Yesu anakulabe m'nzeru ndi mumsinkhu, ndi m'chisomo cha pa Mulungu ndi cha pa anthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

52 Ndipo Yesu analikunka nakula m'nzeru ndi mu msinkhu, ndipo Mulungu ndi anthu omwe ankakondwera naye kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

52 Ndipo Yesu anakula mu nzeru, msinkhu ndi chisomo cha Mulungu ndi anthu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 2:52
6 Mawu Ofanana  

Ndipo mwanayo anakula, nalimbika mu mzimu wake, ndipo iye anali m'mapululu, kufikira masiku akudzionetsa yekha kwa Israele.


Ndipo mwanayo anakula nalimbika, nalikudzala ndi nzeru; ndi chisomo cha Mulungu chinali pa Iye.


Pakuti iye amene atumikira Khristu mu izi akondweretsa Mulungu, navomerezeka ndi anthu.


Ndipo mwanayo Samuele anakulakula, ndipo Yehova ndi anthu omwe anamkomera mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa