Luka 2:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo atate wake ndi amake akamuka chaka ndi chaka ku Yerusalemu ku Paska. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo atate wake ndi amake akamuka chaka ndi chaka ku Yerusalemu ku Paska. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Makolo a Yesu ankapita ku Yerusalemu chaka ndi chaka ku chikondwerero cha Paska. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Chaka chilichonse makolo ake ankapita ku Yerusalemu ku phwando la Paska. Onani mutuwo |