Luka 2:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo mwanayo anakula nalimbika, nalikudzala ndi nzeru; ndi chisomo cha Mulungu chinali pa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo mwanayo anakula nalimbika, nalikudzala ndi nzeru; ndi chisomo cha Mulungu chinali pa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Mwanayo ankakula, nasanduka wamphamvu nkukhalanso wa nzeru zabasi. Ndipo Mulungu ankamudalitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Ndipo Mwanayo anakula nakhala wamphamvu; Iye anadzazidwa ndi nzeru, ndipo chisomo cha Mulungu chinali pa Iye. Onani mutuwo |