Luka 2:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo pamene iwo anatha zonse monga mwa chilamulo cha Ambuye, anabwera ku Galileya, kumzinda kwao, ku Nazarete. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo pamene iwo anatha zonse monga mwa chilamulo cha Ambuye, anabwera ku Galileya, kumudzi kwao, ku Nazarete. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Yosefe ndi Maria atachita zonse potsata Malamulo a Ambuye, adabwerera ku Galileya, kumudzi kwao ku Nazarete. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Yosefe ndi Mariya atachita zonse zimene zinkafunikira ndi lamulo la Ambuye, anabwerera ku Galileya ku mudzi wa Nazareti. Onani mutuwo |