Luka 2:14 - Buku Lopatulika14 Ulemerero ukhale kwa Mulungu Kumwambamwamba, ndi mtendere pansi pano mwa anthu amene akondwera nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ulemerero ukhale kwa Mulungu Kumwambamwamba, ndi mtendere pansi pano mwa anthu amene akondwera nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Ulemerero kwa Mulungu Kumwambamwamba, ndipo pansi pano mtendere pakati pa anthu amene Iye amakondwera nawo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Ulemerero kwa Mulungu mmwambamwamba, ndi mtendere kwa anthu pa dziko lapansi amene Iye akondwera nawo.” Onani mutuwo |