Luka 2:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo dzidzidzi panali pamodzi ndi mngeloyo ambirimbiri a gulu la Kumwamba, natamanda Mulungu, nanena, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo dzidzidzi panali pamodzi ndi mngeloyo ambirimbiri a gulu la Kumwamba, natamanda Mulungu, nanena, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mwadzidzidzi pamodzi ndi mngeloyo padaoneka gulu lalikulu la angelo ena. Ankatamanda Mulungu ndi mau akuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mwadzidzidzi gulu lalikulu la angelo linaonekera pamodzi ndi mngeloyo, kuyamika Mulungu ndi kumati, Onani mutuwo |