Luka 19:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yesu anati kwa iye, Lero chipulumutso chagwera nyumba iyi, popeza iyenso ndiye mwana wa Abrahamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yesu anati kwa iye, Lero chipulumutso chagwera nyumba iyi, popeza iyenso ndiye mwana wa Abrahamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Apo Yesu adamuuza kuti, “Chipulumutso chafika m'banja lino lero, popeza kuti ameneyunso ndi mwana wa Abrahamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yesu anati kwa iye, “Lero chipulumutso chafika mʼnyumba ino, chifukwa munthu uyu nayenso ndi mwana wa Abrahamu. Onani mutuwo |