Luka 19:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pajatu Mwana wa Munthu adabwera kudzafunafuna ndi kudzapulumutsa amene adatayika.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pajatu Mwana wa Munthu anabwera kudzafunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.” Onani mutuwo |