Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 19:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo m'mene anachiona anadandaula onse, nanena, Analowa amchereze munthu ali wochimwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo m'mene anachiona anadandaula onse, nanena, Analowa amchereze munthu ali wochimwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Poona zimenezi, anthu onse adayamba kung'ung'udza. Adati, “Wakakhala kunyumba kwa munthu wochimwa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Anthu onse ataona zimenezi anayamba kungʼungʼudza, nati, “Iye akupita kuti akakhale mlendo wa wochimwa.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:7
11 Mawu Ofanana  

Koma m'mene iwo analilandira, anaderera kwa mwini banja,


ndipo kwa iwo anati, Pitani inunso kumunda, ndipo ndidzakupatsani chimene chili choyenera. Ndipo iwo anapita.


Ndipo Afarisi, pakuona ichi, ananena kwa ophunzira ake, Chifukwa ninji Mphunzitsi wanu alinkudya pamodzi ndi amisonkho ndi ochimwa?


Ndipo Afarisi ndi alembi anadandaula nati, Uyu alandira anthu ochimwa, nadya nao.


Ndipo anafulumira, natsika, namlandira Iye wokondwera.


Ndipo Zakeyo anaimirira nati kwa Ambuye, Taonani, Ambuye, gawo limodzi la zanga zonse zogawika pakati ndipatsa osauka; ndipo ngati ndalanda kanthu kwa munthu monyenga, ndimbwezera kanai.


Ndipo Afarisi ndi alembi ao anang'ung'udza kwa ophunzira ake, nanena, kuti, Bwanji inu mukudya ndi kumwa pamodzi ndi anthu amisonkho ndi ochimwa?


Mwana wa Munthu wafika wakudya ndi wakumwa; ndipo munena, Onani, munthu wosusuka ndi wakumwaimwa vinyo, bwenzi la amisonkho ndi anthu ochimwa!


Koma Mfarisi, amene adamuitana Iye, pakuona, ananena mwa yekha, nati, Akadakhala mneneri uyu akadazindikira ali yani, ndi wotani mkaziyo womkhudza Iye, chifukwa ali wochimwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa