Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 19:30 - Buku Lopatulika

30 nati, Mukani kumudzi uli pandunji panu; m'menemo, polowa, mudzapeza mwana wa bulu womangidwa, pamenepo palibe munthu anakwerapo nthawi iliyonse; mummasule iye nimumtenge.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 nati, Mukani kumudzi uli pandunji panu; m'menemo, polowa, mudzapeza mwana wa bulu womangidwa, pamenepo palibe munthu anakwerapo nthawi iliyonse; mummasule iye nimumtenge.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 naŵauza kuti, “Pitani m'mudzi mukuwonawo. Mukakangoloŵamo mukapeza mwanawabulu ali chimangire, amene munthu sanakwerepo chikhalire. Mukammasule, nkubwera naye kuno.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 “Pitani mʼmudzi uli patsogolo panu, mukakalowa mʼmudzimo, mukapeza mwana wabulu womangiriridwa amene wina aliyense sanakwerepo. Mukamumasule ndi kubwera naye kuno.

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:30
7 Mawu Ofanana  

nanena kwa iwo, Mukani kumudzi wopenyana ndi inu, ndipo pomwepo mudzapeza bulu womangidwa, ndi mwana wake pamodzi naye, masulani iwo, mudze nao kwa Ine.


Ndipo kunali, m'mene anayandikira ku Betefage ndi Betaniya, paphiri lotchedwa la Azitona, anatuma awiri a ophunzira,


Ndipo munthu akati kwa inu, Mummasuliranji? Mudzatero naye, Ambuye amfuna iye.


Ndipo anachoka otumidwawo, napeza monga adanena kwa iwo.


Ndipo tsopano ndakuuzani chisanachitike, kuti pamene chitachitika mukakhulupirire.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa