Luka 19:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo kunali, m'mene anayandikira ku Betefage ndi Betaniya, paphiri lotchedwa la Azitona, anatuma awiri a ophunzira, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo kunali, m'mene anayandikira ku Betefage ndi Betaniya, pa phiri lotchedwa la Azitona, anatuma awiri a ophunzira, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Atafika pafupi ndi midzi ya Betefage ndi Betaniya, pafupi ndi phiri lotchedwa Phiri la Olivi, adatuma ophunzira aŵiri, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Iye atayandikira ku Betifage ndi Betaniya pa phiri lotchedwa Olivi, Iye anatuma awiri a ophunzira nati kwa iwo, Onani mutuwo |