Luka 19:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo munthu akati kwa inu, Mummasuliranji? Mudzatero naye, Ambuye amfuna iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo munthu akati kwa inu, Mummasuliranji? Mudzatero naye, Ambuye amfuna iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Wina akakakufunsani kuti, ‘Mukummasuliranji?’ Mukati, ‘Ambuye ali naye ntchito.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Ngati wina aliyense akakufunsani kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani mukumumasula mwana buluyo?’ Mukamuwuze kuti, ‘Ambuye akumufuna.’ ” Onani mutuwo |