Luka 18:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo anatinso kwa ena amene anadzikhulupirira mwa iwo okha kuti ali olungama, napeputsa onse ena, fanizo ili, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo anatinso kwa ena amene anadzikhulupirira mwa iwo okha kuti ali olungama, napeputsa onse ena, fanizo ili, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Yesu adaŵapheranso fanizo anthu ena amene ankadziyesa olungama nkumanyoza anzao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yesu ananena fanizoli kwa amene amadzikhulupirira mwa iwo okha kuti anali wolungama nanyoza ena onse. Onani mutuwo |