Luka 18:10 - Buku Lopatulika10 Anthu awiri anakwera kunka ku Kachisi kukapemphera; winayo Mfarisi ndi mnzake wamsonkho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Anthu awiri anakwera kunka ku Kachisi kukapemphera; winayo Mfarisi ndi mnzake wamsonkho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adati, “Anthu aŵiri adaapita ku Nyumba ya Mulungu kukapemphera. Wina anali Mfarisi, wina anali wokhometsa msonkho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Anthu awiri anapita ku Nyumba ya Mulungu kukapemphera, wina Mfarisi ndi winayo wolandira msonkho. Onani mutuwo |