Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 18:25 - Buku Lopatulika

25 Pakuti nkwapafupi kwa ngamira ipyole diso la singano koma kwa munthu mwini chuma, kulowa Ufumu wa Mulungu nkwapatali.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Pakuti nkwapafupi kwa ngamira ipyole diso la singano koma kwa munthu mwini chuma, kulowa Ufumu wa Mulungu nkwapatali.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Nkwapafupi kuti ngamira idzere pa kachiboo ka zingano, kupambana kuti munthu wolemera akaloŵe mu Ufumu wa Mulungu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Ndithudi, nʼkwapafupi kuti ngamira idutse pa kabowo ka zingano kusiyana ndi munthu wachuma kulowa mu ufumu wa Mulungu.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:25
5 Mawu Ofanana  

Ndiponso ndinena kwa inu, Nkwapafupi kuti ngamira ipyole diso la singano, koposa mwini chuma kulowa Ufumu wa Kumwamba.


Atsogoleri akhungu inu, akukuntha udzudzu, koma mumeza ngamira.


Pakuti chapafupi nchiti, kunena, Machimo ako akhululukidwa; kapena kunena, Tanyamuka. Nuyende?


Nkwa pafupi kuti ngamira ipyole diso la singano kuposa kuti mwini chuma alowe mu Ufumu wa Mulungu.


Koma akumvawo anati, Tsono ndani angathe kupulumutsidwa?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa