Luka 18:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Yesu pomuona iye anati, Ha! Nkuvutika nanga kwa anthu eni chuma kulowa Ufumu wa Mulungu! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Yesu pomuona iye anati, Ha! Nkuvutika nanga kwa anthu eni chuma kulowa Ufumu wa Mulungu! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Yesu adamuyang'ana, nanena kuti, “Nkwapatali kwambiri kwa anthu achuma kuti akaloŵe mu Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Yesu anamuyangʼana nati, “Nʼkwapatali kwambiri kuti anthu achuma akalowe mu ufumu wa Mulungu! Onani mutuwo |