Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 18:26 - Buku Lopatulika

26 Koma akumvawo anati, Tsono ndani angathe kupulumutsidwa?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Koma akumvawo anati, Tsono ndani angathe kupulumutsidwa?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Anthu amene adamva zimenezi adafunsa kuti, “Tsono nanga angathe kupulumuka ndani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Amene anamva izi anafunsa kuti, “Nanga ndani amene angapulumuke?”

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:26
3 Mawu Ofanana  

Ndipo munthu anati kwa Iye, Ambuye, akupulumutsidwa ndiwo owerengeka kodi? Koma Iye anati kwa iwo,


Pakuti nkwapafupi kwa ngamira ipyole diso la singano koma kwa munthu mwini chuma, kulowa Ufumu wa Mulungu nkwapatali.


Koma Iye anati, Zinthu zosatheka ndi anthu zitheka ndi Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa