Luka 17:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo monga kunakhala masiku a Nowa, momwemo kudzakhalanso masiku a Mwana wa Munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo monga kunakhala masiku a Nowa, momwemo kudzakhalanso masiku a Mwana wa Munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 “Monga momwe zidaachitikira pa nthaŵi ya Nowa, zidzateronso pa nthaŵi ya Mwana wa Munthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 “Monga mmene zinkachitikira nthawi ya Nowa, momwemonso zidzachitikanso nthawi ya Mwana wa Munthu. Onani mutuwo |