Luka 17:25 - Buku Lopatulika25 Koma ayenera ayambe wamva zowawa zambiri nakanidwe ndi mbadwo uno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Koma ayenera athange wamva zowawa zambiri nakanidwe ndi mbadwo uno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Koma Iye ayenera kuti ayambe wamva zoŵaŵa zambiri, ndipo kuti anthu amakono amkane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Koma poyamba ayenera kuzunzika mu zambiri ndi kukanidwa ndi mʼbado uno. Onani mutuwo |