Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 17:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo Yesu anayankha nati, Kodi sanakonzedwe khumi? Koma ali kuti asanu ndi anai aja?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo Yesu anayankha nati, Kodi sanakonzedwe khumi? Koma ali kuti asanu ndi anai aja?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Apo Yesu adati, “Kodi achira aja si khumi? Nanga asanu ndi anai ena aja ali kuti?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Yesu anafunsa kuti, “Kodi amene anachiritsidwa sanalipo khumi? Nanga asanu ndi anayi ena ali kuti?

Onani mutuwo Koperani




Luka 17:17
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti?


Koma anaiwala ntchito zake msanga; sanalindire uphungu wake:


ndipo anagwa nkhope yake pansi kumapazi ake, namyamika Iye; ndipo anali Msamariya ameneyo.


Akubwera kulemekeza Mulungu sanapezeke mmodzi kodi, koma mlendo uyu?


chifukwa kuti, ngakhale anadziwa Mulungu, sanamchitire ulemu wakuyenera Mulungu, ndipo sanamyamike; koma anakhala opanda pake m'maganizo ao, ndipo unada mtima wao wopulukira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa