Luka 17:16 - Buku Lopatulika16 ndipo anagwa nkhope yake pansi kumapazi ake, namyamika Iye; ndipo anali Msamariya ameneyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 ndipo anagwa nkhope yake pansi kumapazi ake, namyamika Iye; ndipo anali Msamariya ameneyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Adagwada nkuŵerama kwambiri pamaso pa Yesu, namthokoza. Koma munthuyo anali Msamariya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Anagwetsa nkhope yake nagwa pa mapazi a Yesu ndi kumuthokoza. Ndipo iye anali Msamariya. Onani mutuwo |