Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 17:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo mmodzi wa iwo, pakuona kuti anachiritsidwa, anabwerera m'mbuyo, nalemekeza Mulungu ndi mau aakulu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo mmodzi wa iwo, pakuona kuti anachiritsidwa, anabwerera m'mbuyo, nalemekeza Mulungu ndi mau akulu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Tsono mmodzi mwa iwo, ataona kuti wachira, adabwerera nayamba kuyamika Mulungu mokweza mau.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Mmodzi wa iwo, ataona kuti wachiritsidwa, anabwerera, nayamika Mulungu ndi mawu okweza.

Onani mutuwo Koperani




Luka 17:15
13 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene anthu a makamu anachiona, anaopa, nalemekeza Mulungu, wakupatsa anthu mphamvu yotere.


Ndipo ananyamuka iye pomwepo, nasenza mphasa, natuluka pamaso pa iwo onse; kotero kuti anadabwa onse, nalemekeza Mulungu, nanena kuti, Zotere sitinazione ndi kale lonse.


Zitapita izi Yesu anampeza mu Kachisi, nati kwa iye, Taona, wachiritsidwa; usachimwenso, kuti chingakugwere choipa choposa.


Koma iye anati, Ndikhulupirira, Ambuye; ndipo anamgwadira Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa