Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 17:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo pakuwaona anati kwa iwo, Pitani, kadzionetseni nokha kwa ansembe. Ndipo kunali, m'kumuka kwao, anakonzedwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo pakuwaona anati kwa iwo, Pitani, kadzionetseni nokha kwa ansembe. Ndipo kunali, m'kumuka kwao, anakonzedwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Pamene Yesu adaŵaona, adaŵauza kuti, “Pitani, kadziwonetseni kwa ansembe.” Pamene iwo ankapita, adachira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Iye atawaona, anati, “Pitani kadzionetseni nokha kwa ansembe.” Ndipo pamene iwo ankapita, anachiritsidwa.

Onani mutuwo Koperani




Luka 17:14
11 Mawu Ofanana  

Potero anatsika, namira mu Yordani kasanu ndi kawiri, monga adanena munthu wa Mulunguyo; ndi mnofu wake unabwera monga mnofu wa mwana wamng'ono, nakonzeka.


Ndipo padzakhala kuti iwo asanaitane Ine, ndidzayankha; ndipo ali chilankhulire, Ine ndidzamva.


Koma Yesu anayankha, nati kwa iye, Balola tsopano: pakuti kuyenera ife kukwaniritsa chilungamo chonse motero. Pamenepo anamlola Iye.


Ndipo Iye anamuuzitsa, kuti asanene kwa munthu aliyense; koma uchoke, nudzionetse wekha kwa wansembe, nupereke nsembe ya pa chikonzedwe chako, monga adalamulira Mose, kukhale umboni kwa iwo.


Koma ngati munthu ayenda usiku, akhumudwa, chifukwa mulibe kuunika mwa iye.


Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.


nati kwa iye, Muka, kasambe m'thamanda la Siloamu (ndilo losandulika, Wotumidwa). Pamenepo anachoka, nasamba, nabwera alikuona.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa