Luka 16:30 - Buku Lopatulika30 Koma anati, Iai, Atate Abrahamu, komatu ngati wina akapita kwa iwo wochokera kwa kufa adzasandulika mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Koma anati, Iai, Atate Abrahamu, komatu ngati wina akapita kwa iwo wochokera kwa kufa adzasandulika mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Iye adati, ‘Iyai, atate Abrahamu, koma wina atauka kwa akufa nkupita kwa iwo, apo adzatembenuka mtima.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 “Iye anati, ‘Ayi, bambo Abrahamu, koma ngati wina ochokera kwa akufa adzapita kwa iwo, adzatembenuka mtima.’ Onani mutuwo |