Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 16:29 - Buku Lopatulika

29 Koma Abrahamu anati, Ali ndi Mose ndi aneneri; amvere iwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Koma Abrahamu anati, Ali ndi Mose ndi aneneri; amvere iwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Koma Abrahamu adati, ‘Iwo ali ndi mabuku a Mose ndi a aneneri. Amvere zam'menemo.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 “Abrahamu anayankha kuti, ‘Ali ndi Mose ndi Aneneri; aleke amvere iwo.’

Onani mutuwo Koperani




Luka 16:29
13 Mawu Ofanana  

Funani inu m'buku la Yehova, nimuwerenge; palibe umodzi wa iye udzasowa, palibe umodzi udzasowa unzake; pakuti pakamwa pa Yehova panena, ndipo mzimu wake wasonkhanitsa iwo.


Kuchilamulo ndi kuumboni! Ngati iwo sanena malinga ndi mau awa, ndithu sadzaona mbandakucha.


Yehova atero, Imani m'njira ndi kuona, funsani za mayendedwe akale, m'menemo muli njira yabwino, muyende m'menemo, ndipo mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu; koma anati, Sitidzayendamo.


Chilamulo ndi aneneri analipo kufikira pa Yohane; kuyambira pamenepo ulalikidwa Uthenga Wabwino wa Ufumu wa Mulungu, ndipo munthu aliyense akangamira kulowamo.


Ndipo anayamba kwa Mose, ndi kwa aneneri onse nawatanthauzira iwo m'malembo onse zinthu za Iye yekha.


Ndipo anapereka kwa Iye buku la Yesaya mneneri. Ndipo m'mene Iye adafunyulula bukulo, anapeza pomwe panalembedwa,


Pakuti Mose, kuyambira pa mibadwo yakale ali nao m'mizinda yonse amene amlalikira, akuwerenga mau ake m'masunagoge masabata onse.


Ndiuzeni, inu akufuna kukhala omvera lamulo, kodi simukumva chilamulo?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa