Luka 16:29 - Buku Lopatulika29 Koma Abrahamu anati, Ali ndi Mose ndi aneneri; amvere iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Koma Abrahamu anati, Ali ndi Mose ndi aneneri; amvere iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Koma Abrahamu adati, ‘Iwo ali ndi mabuku a Mose ndi a aneneri. Amvere zam'menemo.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 “Abrahamu anayankha kuti, ‘Ali ndi Mose ndi Aneneri; aleke amvere iwo.’ Onani mutuwo |