Luka 16:31 - Buku Lopatulika31 Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Koma Abrahamu adamuuza kuti, ‘Ngatitu iwo samvera Mose ndi aneneri, sangathekenso ngakhale wina auke kwa akufa.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 “Anati kwa iye, ‘Ngati iwo samvera Mose ndi Aneneri, sadzakhulupirira ngakhale wina atauka kwa akufa.’ ” Onani mutuwo |