Luka 15:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo anaitana mmodzi wa anyamata, namfunsa, Zinthu izi nzotani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo anaitana mmodzi wa anyamata, namfunsa, Zinthu izi nzotani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Adaitana wantchito mmodzi namufunsa kuti, ‘Kodi kwagwanji?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Ndipo iye anayitana mmodzi wa antchito, namufunsa chimene chimachitika. Onani mutuwo |