Luka 15:25 - Buku Lopatulika25 Koma mwana wake wamkulu anali kumunda. Ndipo pakubwera iye ndi kuyandikira kunyumba, anamva kuimba ndi kuvina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Koma mwana wake wamkulu anali kumunda. Ndipo pakubwera iye ndi kuyandikira kunyumba, anamva kuimba ndi kuvina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 “Koma mwana wake wamkulu uja anali ku munda. Pochokera kumundako, atafika pafupi ndi nyumba, adamva anthu akuimba ndi kuvina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 “Nthawi imeneyi, mwana wake wamkulu uja anali ku munda. Iye atafika pafupi ndi nyumba, anamva anthu akuyimba ndi kuvina. Onani mutuwo |