Luka 15:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo pamene anatha zake zonse, panakhala njala yaikulu m'dziko muja, ndipo iye anayamba kusowa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo pamene anatha zake zonse, panakhala njala yaikulu m'dziko muja, ndipo iye anayamba kusowa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Chitamthera chuma chake chonse, mudaloŵa njala yaikulu m'dziko limeneli, mwakuti iye yemwe adayamba kusauka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Iye atawononga zonse, kunagwa njala yoopsa mʼdziko lonselo ndipo anayamba kusauka. Onani mutuwo |