Luka 15:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo anamuka nadziphatikiza kwa mfumu imodzi ya dziko lija; ndipo uyu anamtumiza kubusa kwake kukaweta nkhumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo anamuka nadziphatikiza kwa mfumu imodzi ya dziko lija; ndipo uyu anamtumiza kubusa kwake kukaweta nkhumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Pamenepo adapita kukakhala nao kwa nzika ina ya m'dzikomo. Nzikayo idamtuma ku busa kukaŵeta nkhumba zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Iye anapita kwa nzika ina ya dzikolo nakakhala naye ndi kumagwira ntchito, amene anamutumiza ku munda kukadyetsa nkhumba. Onani mutuwo |