Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 14:9 - Buku Lopatulika

9 ndipo pakufika iye amene adaitana iwe ndi uyu, adzati kwa iwe, Mpatse uyu malo; ndipo pomwepo udzayamba manyazi kukhala pa mpando wa kuthungo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 ndipo pakufika iye amene adaitana iwe ndi uyu, adzati kwa iwe, Mpatse uyu malo; ndipo pomwepo udzayamba manyazi kukhala pa mpando wa kuthungo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Ndiye iye uja amene adaitana aŵiri nonsenu nkudzakuuza kuti, ‘Pepani, patsani aŵa maloŵa.’ Apo iweyo udzachita manyazi pokakhala pa malo otsika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ngati zitatero, ndiye kuti munthu uja amene anakuyitani inu nonse awiri adzakuwuzani kuti, ‘Mupatseni munthu uyu malo anu.’ Pamenepo inu mudzachita manyazi, pokakhala malo wotsika.

Onani mutuwo Koperani




Luka 14:9
8 Mawu Ofanana  

Pakudza kudzikuza padzanso manyazi; koma nzeru ili ndi odzichepetsa.


Kunyada kutsogolera kuonongeka; mtima wodzikuza ndi kutsogolera kuphunthwa.


Anzeru adzalandira ulemu cholowa chao; koma opusa adzakweza manyazi.


Ndipo pamene Iye anatero, onse aja akutsutsana naye ananyazitsidwa; ndipo anthu onse a m'khamu anakondwera ndi zinthu zonse za ulemererozo zinachitidwa ndi Iye.


Chifukwa chake balani zipatso zakuyenera kulapa mtima, ndipo musayambe kunena mwa inu nokha, Atate wathu tili naye ndiye Abrahamu: pakuti ndinena kwa inu, kuti ali ndi mphamvu Mulungu, mwa miyala iyi, kuukitsira Abrahamu ana.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa