Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 14:8 - Buku Lopatulika

8 Pamene paliponse waitanidwa iwe ndi munthu ku chakudya cha ukwati, usaseama pa mpando waulemu; kuti kapena wina waulemu wakuposa iwe akaitanidwe ndi iye,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Pamene paliponse waitanidwa iwe ndi munthu ku chakudya cha ukwati, usaseama pa mpando waulemu; kuti kapena wina waulemu wakuposa iwe akaitanidwe ndi iye,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 “Wina akakuitana ku phwando la ukwati, usamakhala pa malo aulemu ai, chifukwa mwina kapena adaitananso wina waulemu kuposa iwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 “Pamene wina wakuyitanani ku phwando la ukwati, musakhale pa malo aulemu ayi, chifukwa mwina anayitananso munthu wina wolemekezeka kuposa inu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 14:8
1 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa