Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 14:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo iwo sanathe kumbwezera mau pa zinthu izi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo iwo sanathe kumbwezera mau pa zinthu izi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Iwo adasoŵa poyankha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Ndipo iwo analibe choyankha.

Onani mutuwo Koperani




Luka 14:6
6 Mawu Ofanana  

Ndipo sanalimbike mtima munthu aliyense kumfunsa kanthu kuyambira tsiku lomwelo.


Ndipo pamene Iye anatero, onse aja akutsutsana naye ananyazitsidwa; ndipo anthu onse a m'khamu anakondwera ndi zinthu zonse za ulemererozo zinachitidwa ndi Iye.


Ndipo sanakhoze kugwira mauwo pamaso pa anthu; ndipo anazizwa ndi kuyankha kwake, nakhala chete.


Pakuti sanalimbenso mtima kumfunsa Iye kanthu kena.


Pakuti Ine ndidzakupatsani inu kamwa ndi nzeru, zimene adani anu onse sadzatha kuzikana kapena kuzitsutsa.


Ndipo sanathe kuipambana nzeru ndi Mzimu amene analankhula naye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa