Luka 14:14 - Buku Lopatulika14 ndipo udzakhala wodala; chifukwa iwo alibe chakubwezera iwe mphotho; pakuti idzabwezedwa mphotho pa kuuka kwa olungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 ndipo udzakhala wodala; chifukwa iwo alibe chakubwezera iwe mphotho; pakuti idzabwezedwa mphotho pa kuuka kwa olungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Apo udzakhala wodala, chifukwa iwo alibe kanthu koti nkukubwezera. Mulungu ndiye adzakubwezera, pamene anthu olungama adzauka kwa akufa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pamenepo udzakhala wodala, chifukwa iwo sangakubwezere kanthu, koma Mulungu ndiye adzakubwezera pa chiukitso cha olungama.” Onani mutuwo |