Luka 14:13 - Buku Lopatulika13 Koma pamene ukonza phwando uitane aumphawi, opunduka, otsimphina, akhungu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma pamene ukonza phwando uitane aumphawi, opunduka, otsimphina, akhungu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma iwe ukamakonza phwando, uziitana amphaŵi, otsimphina, opunduka ndi akhungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Koma ukakonza phwando, itana anthu osauka, ofa ziwalo, olumala ndi osaona. Onani mutuwo |
Ndipo mukondwere pamaso pa Yehova Mulungu wanu, inu ndi ana anu aamuna, ndi ana anu aakazi, ndi antchito anu aamuna, ndi antchito anu aakazi, ndi Mlevi wokhala m'mudzi mwanu, ndi mlendo, ndi mwana wamasiye, ndi mkazi wamasiye, okhala pakati pa inu, m'malo amene Yehova Mulungu wanu adzasankha kukhalitsako dzina lake.