Luka 13:5 - Buku Lopatulika5 Ndinena kwa inu, Iaitu; koma ngati simutembenuka mtima, mudzaonongeka nonse chimodzimodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndinena kwa inu, Iaitu; koma ngati simutembenuka mtima, mudzaonongeka nonse chimodzimodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Iyai, koma mukapanda kutembenuka mtima, inunso mudzaonongedwa ngati iwo aja.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ine ndikuti, ayi! Koma ngati inu simutembenuka mtima, inunso mudzawonongeka nonse.” Onani mutuwo |