Luka 13:4 - Buku Lopatulika4 Kapena iwo aja khumi ndi asanu ndi atatu, amene nsanja yaitali ya mu Siloamu inawagwera, ndi kuwapha; kodi muyesa kuti iwo anali olakwa koposa anthu onse akukhala m'Yerusalemu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Kapena iwo aja khumi ndi asanu ndi atatu, amene nsanja yaitali ya m'Siloamu inawagwera, ndi kuwapha; kodi muyesa kuti iwo anali olakwa koposa anthu onse akukhala m'Yerusalemu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Nanga anthu aja 18 amene nyumba yosanja idaŵagwera ku Siloamu nkuŵapha? Kodi mukuyesa kuti iwowo anali ophwanya malamulo koposa anthu ena onse okhala m'Yerusalemu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kapena anthu 18 aja amene anafa nsanja ya Siloamu itawagwera, kodi mukuganiza kuti iwo aja anali ochimwa kwambiri kuposa onse amene amakhala mu Yerusalemu? Onani mutuwo |