Luka 13:3 - Buku Lopatulika3 Ndinena kwa inu, Iaitu; koma ngati inu simutembenuka mtima, mudzaonongeka nonse momwemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndinena kwa inu, Iaitu; koma ngati inu simutembenuka mtima, mudzaonongeka nonse momwemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Iyai, koma mukapanda kutembenuka mtima, inunso mudzaonongedwa ngati iwo aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ine ndikuti, ayi! Koma ngati inu simutembenuka mtima, inunso mudzawonongeka nonse. Onani mutuwo |