Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 13:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo munthu anati kwa Iye, Ambuye, akupulumutsidwa ndiwo owerengeka kodi? Koma Iye anati kwa iwo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo munthu anati kwa Iye, Ambuye, akupulumutsidwa ndiwo owerengeka kodi? Koma Iye anati kwa iwo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Munthu wina adamufunsa kuti, “Ambuye, kodi adzapulumuka ndi anthu oŵerengeka okha?” Yesu adayankha kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Wina anamufunsa Iye kuti, “Ambuye, kodi ndi anthu ochepa okha amene adzapulumutsidwe?” Iye anawawuza kuti,

Onani mutuwo Koperani




Luka 13:23
12 Mawu Ofanana  

Ndipo ophunzira, pamene anamva, anazizwa kwambiri, nanena, Ngati nkutero angapulumuke ndani?


Chomwecho omalizira adzakhala oyamba, ndipo oyamba adzakhala omalizira.


Pakuti oitanidwa ndiwo ambiri, koma osankhidwa ndiwo owerengeka.


Pakuti chipata chili chopapatiza, ndi ichepetsa njirayo yakumuka nayo kumoyo, ndimo akuchipeza chimenecho ali owerengeka.


Ndipo Iye anapita pakati pa mizinda ndi midzi, naphunzitsa, nayenda ulendo kunkabe ku Yerusalemu.


Yesetsani kulowa pa khomo lopapatiza; chifukwa anthu ambiri, ndikuuzani, adzafunafuna kulowamo, koma sadzakhoza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa