Luka 13:24 - Buku Lopatulika24 Yesetsani kulowa pa khomo lopapatiza; chifukwa anthu ambiri, ndikuuzani, adzafunafuna kulowamo, koma sadzakhoza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Yesetsani kulowa pa khomo lopapatiza; chifukwa anthu ambiri, ndikuuzani, adzafunafuna kulowamo, koma sadzakhoza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 “Yesetsani kuloŵera pa khomo lophaphatiza, pakuti kunena zoona anthu ambiri adzafuna kuloŵa, koma adzalephera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 “Yesetsani kulowa pa khomo lopapatiza, chifukwa ndikukuwuzani kuti ambiri adzafuna kulowa koma sadzatha kutero. Onani mutuwo |