Luka 13:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo Iye anapita pakati pa mizinda ndi midzi, naphunzitsa, nayenda ulendo kunkabe ku Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo Iye anapita pakati pa mizinda ndi midzi, naphunzitsa, nayenda ulendo kunkabe ku Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Pa ulendo wake wopita ku Yerusalemu, Yesu ankayendera mizinda ndi midzi akuphunzitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ndipo Yesu anayendayenda mʼmizinda ndi mʼmidzi, kumaphunzitsa pamene Iye ankapita ku Yerusalemu. Onani mutuwo |