Luka 13:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo anaika manja ake pa iye; ndipo pomwepo anaongoledwa, nalemekeza Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo anaika manja ake pa iye; ndipo pomwepo anaongoledwa, nalemekeza Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Adamsanjika manja, ndipo pompo maiyo adaongoka, nayamba kutamanda Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kenaka anasanjika manja ake pa iye, ndipo nthawi yomweyo anawongoka nayamika Mulungu. Onani mutuwo |