Luka 13:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Yesu m'mene anamuona, anamuitana, nanena naye, Mkaziwe, wamasulidwa kudwala kwako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Yesu m'mene anamuona, anamuitana, nanena naye, Mkaziwe, wamasulidwa kudwala kwako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pamene Yesu adamuwona, adamuitana namuuza kuti, “Mai inu, mwamasuka ku matenda anu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yesu atamuona anamuyitana kutsogolo ndipo anati kwa iye, “Amayi, mwamasulidwa ku mavuto.” Onani mutuwo |