Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 12:51 - Buku Lopatulika

51 Kodi muyesa kuti ndinadzera kudzapatsa mtendere padziko lapansi? Ndinena kwa inu, Iaitu, komatu kutsutsana;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

51 Kodi muyesa kuti ndinadzera kudzapatsa mtendere pa dziko lapansi? Ndinena kwa inu, Iaitu, komatu kutsutsana;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

51 Kodi mukuyesa kuti ndidadzapereka mtendere pansi pano? Iyai, kunena zoona, osati mtendere koma kugaŵikana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

51 Kodi mukuganiza kuti Ine ndinabwera kudzabweretsa mtendere pa dziko lapansi? Ayi, Ine ndikukuwuzani kuti, ndinabweretsa kugawikana.

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:51
8 Mawu Ofanana  

Pamenepo ndinadula ndodo yanga ina, ndiyo Chomanganitsa, kuti ndithetse chibale cha pakati pa Yuda ndi Israele.


Ine ndinadzera kuponya moto padziko lapansi; ndipo ndifunanji ngati unatha kuyatsidwa?


pakuti kuyambira tsopano adzakhala m'nyumba imodzi anthu asanu, atatu adzatsutsana ndi awiri, ndi awiri adzatsutsana ndi atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa