Luka 12:50 - Buku Lopatulika50 Koma ndili ndi ubatizo ndikabatizidwe nao; ndipo ndikanikizidwa Ine kufikira ukatsirizidwa! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Koma ndili ndi ubatizo ndikabatizidwe nao; ndipo ndikanikizidwa Ine kufikira ukatsirizidwa! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Koma ndiyenera kuyamba ndaloŵa m'masautso akulu, ndipo mtima wanga sukhazikika mpaka zitachitika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Koma Ine ndiyenera kubatizidwa, ndipo ndikusautsika mu mtima mpaka utachitika! Onani mutuwo |