Luka 12:40 - Buku Lopatulika40 Khalani okonzeka inunso; chifukwa nthawi imene simulingirira, Mwana wa Munthu akudza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Khalani okonzeka inunso; chifukwa nthawi imene simulingirira, Mwana wa Munthu akudza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Choncho inunso khalani okonzeka, pakuti Mwana wa Munthu adzabwera pa nthaŵi imene simukuyembekeza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Inunso muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa ora limene simukumuyembekezera Iye.” Onani mutuwo |