Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 12:40 - Buku Lopatulika

40 Khalani okonzeka inunso; chifukwa nthawi imene simulingirira, Mwana wa Munthu akudza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Khalani okonzeka inunso; chifukwa nthawi imene simulingirira, Mwana wa Munthu akudza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Choncho inunso khalani okonzeka, pakuti Mwana wa Munthu adzabwera pa nthaŵi imene simukuyembekeza.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Inunso muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa ora limene simukumuyembekezera Iye.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:40
10 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake lakufika Ambuye wanu.


Chifukwa chake khalani inunso okonzekeratu; chifukwa munthawi m'mene simuganizira, Mwana wa Munthu adzadza.


Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake, kapena nthawi yake.


Ndipo chitani ichi, podziwa inu nyengo, kuti tsopano ndiyo nthawi yabwino yakuuka kutulo; pakuti tsopano chipulumutso chathu chili pafupi koposa pamene tinayamba kukhulupirira.


Koma valani inu Ambuye Yesu Khristu, ndipo musaganizire za thupi kuchita zofuna zake.


chifukwa chake tsono tisagone monga otsalawo, komatu tidikire, ndipo tisaledzere.


Tikondwere, tisekerere, ndipo tipatse ulemerero kwa Iye; pakuti wadza ukwati wa Mwanawankhosa; ndipo mkazi wake wadzikonzera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa