Luka 12:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo Petro anati, Ambuye, kodi fanizo ili mwalinena kwa ife, kapena kwa onse? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo Petro anati, Ambuye, kodi fanizo ili mwalinena kwa ife, kapena kwa onse? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Pamenepo Petro adati, “Ambuye, kodi fanizoli mukuphera ife tokha, kapena mukuuza onse?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Petro anafunsa kuti, “Kodi mukunena fanizoli kwa ife, kapena kwa aliyense?” Onani mutuwo |