Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 12:39 - Buku Lopatulika

39 Koma zindikirani ichi, kuti mwini nyumba akadadziwa nthawi yake yakudza mbala, akadadikira, ndipo sakadalola nyumba yake ibooledwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Koma zindikirani ichi, kuti mwini nyumba akadadziwa nthawi yake yakudza mbala, akadadikira, ndipo sakadalola nyumba yake ibooledwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 “Koma kumbukirani kuti, mwini nyumba akadadziŵiratu nthaŵi yoti mbala ifika, sibwenzi atalola kuti ithyole nyumba yake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Koma zindikirani izi: Ngati mwini nyumba akanadziwa ora limene mbala ibwera, sakanalola kuti nyumba yake ithyoledwe.

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:39
7 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake dikirani, pakuti simudziwa tsiku lake lakufika Ambuye wanu.


Musadzikundikire nokha chuma padziko lapansi, pamene njenjete ndi dzimbiri ziononga; ndi pamene mbala ziboola ndi kuba:


Koma tsiku la Ambuye lidzadza ngati mbala; m'mene miyamba idzapita ndi chibumo chachikulu, ndi zam'mwamba zidzakanganuka ndi kutentha kwakukulu, ndipo dziko ndi ntchito zili momwemo zidzatenthedwa.


(Taonani, ndidza ngati mbala. Wodala iye amene adikira, nasunga zovala zake, kuti angayende wausiwa, nangapenye anthu usiwa wake.)


Chifukwa chake kumbukira umo unalandira nunamvamo; nusunge nulape. Ukapanda kudikira tsono, ndidzafika ngati mbala, ndipo sudzazindikira nthawi yake ndidzadza pa iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa