Luka 12:39 - Buku Lopatulika39 Koma zindikirani ichi, kuti mwini nyumba akadadziwa nthawi yake yakudza mbala, akadadikira, ndipo sakadalola nyumba yake ibooledwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Koma zindikirani ichi, kuti mwini nyumba akadadziwa nthawi yake yakudza mbala, akadadikira, ndipo sakadalola nyumba yake ibooledwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 “Koma kumbukirani kuti, mwini nyumba akadadziŵiratu nthaŵi yoti mbala ifika, sibwenzi atalola kuti ithyole nyumba yake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Koma zindikirani izi: Ngati mwini nyumba akanadziwa ora limene mbala ibwera, sakanalola kuti nyumba yake ithyoledwe. Onani mutuwo |