Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 12:34 - Buku Lopatulika

34 Pakuti kumene kuli chuma chanu, komweko kudzakhalanso mtima wanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Pakuti kumene kuli chuma chanu, komweko kudzakhalanso mtima wanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Pajatu kumene kuli chuma chako, mtima wakonso kokhala nkomweko.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Popeza kumene kuli chuma chanu, mtima wanunso udzakhala komweko.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:34
4 Mawu Ofanana  

pakuti kumene kuli chuma chako, komwe udzakhala mtima wakonso.


Khalani odzimangira m'chuuno, ndipo nyali zanu zikhale zoyaka;


Pakuti ufulu wathu uli Kumwamba; kuchokera komwenso tilindirira Mpulumutsi, Ambuye Yesu Khristu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa