Luka 12:32 - Buku Lopatulika32 Musaopa, kagulu ka nkhosa inu; chifukwa Atate wanu akonda kukupatsani Ufumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Musaopa, kagulu ka nkhosa inu; chifukwa Atate wanu akonda kukupatsani Ufumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 “Inu nkhosa zanga, ngakhale muli oŵerengeka, musaope, pakuti kudakomera Atate anu kuti akupatseni Ufumu wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 “Musachite mantha, inu kagulu kankhosa, pakuti zinakondweretsa Atate anu kuti akupatseni ufumu. Onani mutuwo |